Takulandilani kuno ku kkps omwe
ndikhulupilira kuti akhalanso malo anu pomwe mudzatha
kugawana nane zina ndi zina. Ndicholinga changa kuti malo ano
athe kufikila kwaiwo omwe akufuna kudziwa kumene zamakina a
kompiyuta ndikwaena odziwa kale pofuna kupititsa patsogolo
chitukuko cha dziko lathu la Malawi. Ndikufunirani zonse zabwino ndipo
ndigawilerni maganizo anu kuti ndithe kukutumikilani bwino.
Maganizo
anu ndi otani pazamavuto aku Zimbabwe ndi Malawi?
Ena akuti kuthetsa mavuto aku Zimbabwe nkovuta
kwambiri ndipo aku Malawi, nkosavuta.Inu
mukuti chani pankhaniyi? Ndigawireni
maganizo anu.
Zolembedwa
zonse ndizotetezedwa. Muli ololedwa kugwiritsa ntchito magawo onse
amalo ano posasowa chilolezo china chili chonse koma mukupemphedwa
kunena komwe mwazitenga ku Tasha
Communications.